Yeremiya 3:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo Yehova anati kwa ine, Israele wobwerera anadzionetsa wolungama kopambana ndi Yuda wonyenga. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo Yehova anati kwa ine, Israele wobwerera anadzionetsa wolungama kopambana ndi Yuda wonyenga. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adandiwuzanso kuti, “Israele wosakhulupirika uja kupalamula kwake nkochepa, kuyerekeza ndi Yuda wosakhulupirika uja. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova anandiwuza kuti, “Kusakhulupirika kwa Israeli nʼkochepa kuyerekeza ndi kusakhulupirika kwa Yuda. Onani mutuwo |