Yeremiya 3:4 - Buku Lopatulika4 Kodi kuyambira tsopano sudzafuulira kwa Ine, Atate wanga, wotsogolera ubwana wanga ndinu? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Kodi kuyambira tsopano sudzafuulira kwa Ine, Atate wanga, wotsogolera ubwana wanga ndinu? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Kodi si tsopano apa wakhala ukundiwuza kuti, ‘Atate, ndinu bwenzi la unyamata wanga,’ numadzifunsa kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Kodi iwe siposachedwa pomwepa pamene wanena kuti, ‘Abambo anga, Inu bwenzi langa la unyamata wanga, Onani mutuwo |