Yeremiya 27:1 - Buku Lopatulika1 Poyamba kukhala mfumu Zedekiya mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, mau awa anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti, Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Poyamba kukhala mfumu Yehoyakimu mwana wake wa Yosiya, mfumu ya Yuda, mau awa anadza kwa Yeremiya kuchokera kwa Yehova, kuti, Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Pamene Zedekiya, mwana wa Yosiya mfumu ya ku Yuda adayamba kulamulira, Chauta adalankhula ndi Yeremiya namuuza kuti, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Zedekiya mwana wa Yosiya, mfumu ya ku Yuda, atangoyamba kulamulira, Yehova anawuza Yeremiya kuti, Onani mutuwo |