Yeremiya 26:24 - Buku Lopatulika24 Koma dzanja la Ahikamu mwana wa Safani linali ndi Yeremiya, kuti asampereke m'manja a anthu kuti amuphe. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 Koma dzanja la Ahikamu mwana wa Safani linali ndi Yeremiya, kuti asampereke m'manja a anthu kuti amuphe. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Koma Ahikamu mwana wa Safani ndiye adatchinjiriza Yeremiya, motero sadaperekedwe kwa anthu kuti amuphe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Koma Ahikamu mwana wa Safani ndiye anateteza Yeremiya, motero sanamupereke kwa anthu kuti amuphe. Onani mutuwo |