Yeremiya 22:8 - Buku Lopatulika8 Ndipo amitundu ambiri adzapita pa mzinda uwu, nadzati yense kwa mnzake, Yehova anatero nao mzinda waukulu uwu chifukwa ninji? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 Ndipo amitundu ambiri adzapita pa mudzi uwu, nadzati yense kwa mnzake, Yehova anatero nao mudzi waukulu uwu chifukwa ninji? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 “Pamene anthu a mitundu ina adzadutse pa mzinda umenewu, azidzafunsana kuti, ‘Kodi chifukwa chiyani Chauta adaononga chotere mzinda waukuluwu?’ Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 “Pamene anthu a mitundu ina adzadutsa pa mzinda umenewu adzafunsana kuti, ‘Chifukwa chiyani Yehova wachita chinthu chotere pa mzinda waukuluwu?’ Onani mutuwo |