Yeremiya 22:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo adzayankha, Chifukwa anasiya pangano la Yehova Mulungu wao, ndi kugwadira milungu ina, ndi kuitumikira. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo adzayankha, Chifukwa anasiya pangano la Yehova Mulungu wao, ndi kugwadira milungu ina, ndi kuitumikira. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Yankho lake lidzakhala lakuti, ‘Nchifukwa chakuti anthu akewo adasiya chipangano chimene adapangana ndi Chauta, Mulungu wao. Adayamba kupembedza milungu ina ndi kumaitumikira.’ ” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo yankho lake lidzakhala lakuti, ‘Chifukwa anasiya pangano limene anapangana ndi Yehova Mulungu wawo ndipo anapembedza ndi kutumikira milungu ina.’ ” Onani mutuwo |