Yeremiya 2:5 - Buku Lopatulika5 atero Yehova, Atate anu apeza chosalungama chanji mwa Ine, kuti andichokera kunka kutali, natsata zachabe, nasanduka achabe? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 atero Yehova, Atate anu apeza chosalungama chanji mwa Ine, kuti andichokera kunka kutali, natsata zachabe, nasanduka achabe? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Iye akukufunsani kuti, “Kodi makolo anu adandipeza ncholakwa chanji kuti andithaŵe? Adatsata milungu yachabechabe, iwonso nkusanduka achabechabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Yehova akuti, “Kodi makolo anu anandipeza nʼcholakwa chanji, kuti andithawe? Iwo anatsata milungu yachabechabe, nawonso nʼkusanduka achabechabe. Onani mutuwo |