Yeremiya 2:16 - Buku Lopatulika16 Ananso a Nofi ndi a Tapanesi, anaswa pakati pamutu pako. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ananso a Nofi ndi a Tapanesi, anaswa pakati pamtu pako. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Aejipito a ku Memfisi ndi a ku Tapanesi akuphwanyani mitu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Ndiponso Aigupto a ku Mefisi ndi a ku Tapanesi akuphwanyani mitu. Onani mutuwo |