Yeremiya 2:17 - Buku Lopatulika17 Kodi sunadzichitire ichi iwe wekha popeza unasiya Yehova Mulungu wako, pamene anatsogolera iwe panjira? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201417 Kodi sunadzichitira ichi iwe wekha popeza unasiya Yehova Mulungu wako, pamene anatsogolera iwe panjira? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa17 Zimenezi zakuwonekerani chifukwa mudasiya Chauta, Mulungu wanu, pamene Iye adakuikani pa njira yabwino. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero17 Zimenezitu zakuchitikirani chifukwa munasiya Yehova Mulungu wanu pamene Iye ankakutsogolerani pa njira yanu? Onani mutuwo |