Yeremiya 2:11 - Buku Lopatulika11 Kodi mtundu wa anthu unasintha milungu yao, imene siili milungu? Koma anthu anga anasintha ulemerero wao ndi chosapindula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Kodi mtundu wa anthu unasintha milungu yao, imene siili milungu? Koma anthu anga anasintha ulemerero wao ndi chosapindula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene udasinthapo milungu yake, ngakhale kuti si milungu konse? Komabe anthu anga asinthitsa Mulungu wao waulemerero ndi milungu yachabechabe. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Kodi ulipo mtundu wa anthu uliwonse umene unasinthapo milungu yake? (Ngakhale kuti si milungu nʼkomwe). Koma anthu anga asinthitsa Mulungu wawo waulemerero ndi mafano achabechabe. Onani mutuwo |