Yeremiya 2:10 - Buku Lopatulika10 Pakuti pitani ku zisumbu za Kitimu nimuone; tumizani ku Kedara nimulingalire bwino; nimuone ngati chinalipo chotere. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Pakuti pitani ku zisumbu za Kitimu nimuone; tumizani ku Kedara nimulingalire bwino; nimuone ngati chinalipo chotere. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Pitani chakuzambwe, ku chilumba cha Kitimu, mukaone, tumani anthu chakuvuma, ku Kedara, akafufuze. Mudzaona kuti zoterezi sizidachitikepo nkale lonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Pitani kumadzulo ku chilumba cha Kitimu, ndipo mukaone, tumizani anthu ku Kedara kuti akafufuze bwino; ndipo muona kuti zinthu zoterezi sizinachitikepo nʼkale lomwe: Onani mutuwo |