Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 2:12 - Buku Lopatulika

12 Muzizwe pamenepo, miyamba inu, muope kwambiri, mukhale ouma, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

12 Muzizwe pamenepo, miyamba inu, muope kwambiri, mukhale ouma, ati Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

12 Inu maiko akumwamba, dabwa nazoni zimenezi, njenjemerani ndi mantha, akuterotu Chauta.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

12 Inu mayiko akumwamba, dabwani ndi zimenezi, ndipo njenjemerani ndi mantha aakulu,” akutero Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 2:12
10 Mawu Ofanana  

Imvani, miyamba inu, tchera makutu, iwe dziko lapansi, chifukwa Yehova wanena, Ndakulitsa ndipo ndalera ana, ndipo iwo anandipandukira Ine.


Khalani ndi kudabwa; sangalalani ndi kukhala akhungu; iwo aledzera, koma si ndi vinyo, ali dzandidzandi; koma si ndi chakumwa chaukali.


Chifukwa chake atero Yehova; Funsanitu m'mitundu, ndani wamva zotero; namwali wa Israele wachita chinthu choopsetsa kwambiri.


Iwe dziko, dziko, dziko lapansi, tamvera mau a Yehova.


Ndinaona dziko lapansi, ndipo taona, linali lopasuka lopanda kanthu; ndipo ndinaona kumwamba, kunalibe kuunika.


Tamva, dziko lapansi iwe; taona, Ine ndidzatengera choipa pa anthu awa, chipatso cha maganizo ao, pakuti sanamvere mau anga, kapena chilamulo changa, koma wachikana.


Tamverani, mapiri inu, chitsutsano cha Yehova, ndi inu maziko olimba a dziko lapansi; pakuti Yehova ali nacho chitsutsano ndi anthu ake, ndipo adzatsutsana ndi Israele.


Ndipo ora lachisanu ndi chimodzi panali mdima padziko lonse, kufikira ora lachisanu ndi chinai.


Kumwamba kutchere khutu, ndipo ndidzanena; ndi dziko lapansi limve mau a m'kamwa mwanga.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa