Yeremiya 19:3 - Buku Lopatulika3 nuti, Tamvani mau a Yehova, inu mafumu a Yuda, ndi okhala mu Yerusalemu; Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero, Taonani, ndidzatengera malo ano choipa, chimene aliyense adzachimva, makutu ake adzachita woo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 nuti, Tamvani mau a Yehova, inu mafumu a Yuda, ndi okhala m'Yerusalemu; Yehova wa makamu, Mulungu wa Israele atero, Taonani, ndidzatengera malo ano choipa, chimene aliyense adzachimva, makutu ake adzachita woo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ukanene kuti, Inu mafumu a ku Yuda ndi onse okhala ku Yerusalemu, imvani mau a Chauta. Chauta Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israele, akuti, ‘Ndidzagwetsa tsoka loopsa pa malo ano, kotero kuti aliyense amene adzamve adzadzidzimuka kwambiri. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Ukanene kuti, ‘Imvani mawu a Yehova, inu mafumu a ku Yuda ndi anthu a ku Yerusalemu. Yehova Wamphamvuzonse, Mulungu wa Israeli, akuti: Tamverani! Ine ndibweretsa mavuto pa malo pano mwakuti aliyense amene adzamve adzadzidzimuka. Onani mutuwo |