Yeremiya 19:4 - Buku Lopatulika4 Chifukwa andisiya Ine, nayesa malo ano achilendo, nafukizira m'menemo milungu ina, imene sanaidziwe, iwowa, ndi makolo ao ndi mafumu a Yuda; nadzaza malo ano ndi mwazi wa osachimwa; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chifukwa andisiya Ine, nayesa malo ano achilendo, nafukizira m'menemo milungu ina, imene sanaidziwe, iwowa, ndi makolo ao ndi mafumu a Yuda; nadzaza malo ano ndi mwazi wa osachimwa; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Anthu andikana Ine, ndipo aipitsa malo ano. Akhala akufukiza lubani kwa milungu yachilendo imene iwowo, makolo ao ndiponso mafumu a ku Yuda sadaidziŵe. Ndipo pa malo ano adakhetserapo magazi a anthu osachimwa. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Pakuti anthu andikana Ine ndipo ayipitsa malo ano. Afukiza lubani pa malo ano kwa milungu imene iwo ngakhale makolo awo ngakhalenso mafumu a ku Yuda sanayidziwe. Iwo adzaza malowa ndi magazi a anthu osalakwa. Onani mutuwo |