Yeremiya 18:9 - Buku Lopatulika9 Ndipo mphindi imene ndikanenera mtundu, ndi ufumu, kuti ndimangitse mudzi wake ndi kuuoka; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Ndipo mphindi imene ndikanenera mtundu, ndi ufumu, kuti ndimangitse mudzi wake ndi kuuoka; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Momwemonso ngati ndifuna kuyambitsa ndi kukhazikitsa mtundu kapena ufumu wina, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Ndipo ngati ndilengeza kuti ndikufuna kumanga ndi kukhazikitsa mtundu wa anthu kapena ufumu. Onani mutuwo |