Yeremiya 18:8 - Buku Lopatulika8 ngati mtundu umene, ndaunenera, udzatembenuka kuleka choipa chao, ndidzaleka choipacho ndidati ndiwachitire. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 ngati mtundu umene, ndaunenera, udzatembenuka kuleka choipa chao, ndidzaleka choipacho ndidati ndiwachitire. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 ngati mtundu umene ndauchenjezawo uleka machimo ake, ndiye kuti sindidzaulanga monga m'mene ndinkaganizira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 ndipo ngati mtundu wa anthu umene ndawuchenjezawo ulapa zoyipa zawo, ndiye kuti Ine ndidzaleka ndipo sindidzabweretsa pa anthuwo mavuto amene ndinakonzekera kuwachitira. Onani mutuwo |
Ndipo iwe wobadwa ndi munthu, unene ndi ana a anthu a mtundu wako, Cholungama cha wolungama sichidzamlanditsa tsiku la kulakwa kwake, ndi kunena za choipa cha woipa, sadzagwa nacho tsiku lakubwerera iye kuleka choipa chake; ndi munthu wolungama sadzakhoza kukhala ndi moyo ndi chilungamo chake tsiku lakuchimwa iye.