Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 17:7 - Buku Lopatulika

7 Wodala munthu amene akhulupirira Yehova, amene chikhulupiriro chake ndi Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Wodala munthu amene akhulupirira Yehova, amene chikhulupiriro chake ndi Yehova.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 “Koma ndi wodala munthu wokhulupirira Chauta, amene amagonera pa Chautayo.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 “Koma ndi wodala munthu amene amadalira Yehova, amene amatsamira pa Iye.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 17:7
16 Mawu Ofanana  

Iwo akukhulupirira Yehova akunga phiri la Ziyoni, losasunthika, likhazikika kosatha.


Wodala munthu amene akhala naye Mulungu wa Yakobo kuti amthandize, chiyembekezo chake chili pa Yehova, Mulungu wake.


Mpsompsoneni Mwanayo, kuti angakwiye, ndipo mungatayike m'njira ukayaka pang'ono pokha mkwiyo wake. Odala onse akumkhulupirira Iye.


Iwowa anagonjeka, nagwa; koma ife tauka, ndipo takhala chilili.


Talawani, ndipo onani kuti Yehova ndiye wabwino; wodala munthuyo wakukhulupirira Iye.


Wodala munthuyo wakuyesa Yehova wokhulupirika; wosasamala odzikuza, ndi opatukira kubodza.


Pakuti Inu ndinu chiyembekezo changa, Ambuye Yehova; mwandikhalira wokhulupirika kuyambira ubwana wanga.


Yehova wa makamu, wodala munthu wakukhulupirira Inu.


Wolabadira mau adzapeza bwino; ndipo wokhulupirira Yehova adala.


Chifukwa chake Yehova adzadikira, kuti akukomereni mtima, ndipo chifukwa chake Iye adzakuzidwa, kuti akuchitireni inu chifundo; pakuti Yehova ndiye Mulungu wa chiweruziro; odala ali onse amene amdikira Iye.


ndikakonzere iwo amene alira maliro mu Ziyoni, ndi kuwapatsa chovala kokometsa m'malo mwa phulusa, mafuta akukondwa m'malo mwa maliro, chovala cha matamando m'malo mwa mzimu wopsinjika; kuti iwo atchedwe mitengo ya chilungamo yakuioka Yehova, kuti Iye alemekezedwe.


Pakuti ndidzakupulumutsatu ndipo sudzagwa ndi lupanga, koma udzakhala nao moyo wako ngati chofunkha, pakuti wandikhulupirira Ine, ati Yehova.


Nebukadinezara ananena, nati, Alemekezedwe Mulungu wa Sadrake, Mesaki, ndi Abedenego, amene anatuma mthenga wake, napulumutsa atumiki ake omkhulupirira Iye, nasanduliza mau a ine mfumu, napereka matupi ao kuti asatumikire kapena kulambira mulungu wina yense, koma Mulungu waowao.


Koma ndidzasiya pakati pako anthu ozunzika ndi osauka, ndipo iwo adzakhulupirira dzina la Yehova.


kuti ife amene tinakhulupirira Khristu kale tikayamikitse ulemerero wake.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa