Yeremiya 16:3 - Buku Lopatulika3 Pakuti Yehova atero za ana aamuna ndi za ana aakazi akubadwa m'malo muno, ndi za amai anawabala iwo, ndi za atate ao anawabala iwo m'dziko muno: Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Pakuti Yehova atero za ana amuna ndi za ana akazi akubadwa m'malo muno, ndi za amai anawabala iwo, ndi za atate ao anawabala iwo m'dziko muno: Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Ndithu kunena za ana aamuna kapena ana aakazi obadwira kuno, kapenanso za amai ao ndi atate ao amene adabereka anawo m'dziko muno, Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 pakuti ana aamuna ndi ana aakazi obadwira mʼdziko muno, komanso amayi awo ndi abambo awo amene anabereka anawo mʼdziko muno, Onani mutuwo |