Yeremiya 14:4 - Buku Lopatulika4 Chifukwa cha nthaka yochita ming'alu, pakuti panalibe mvula padziko, olima ali ndi manyazi, afunda mitu yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20144 Chifukwa cha nthaka yochita ming'alu, pakuti panalibe mvula padziko, olima ali ndi manyazi, afunda mitu yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa4 Pansi mpouma kotheratu, poti kulibe mvula. Alimi akuchita manyazi, ndipo adziphimba kumaso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero4 Popeza pansi pawumiratu chifukwa kulibe madzi, alimi ali ndi manyazi ndipo amphimba nkhope zawo. Onani mutuwo |