Yeremiya 14:5 - Buku Lopatulika5 Inde, mbawalanso ya m'thengo ibala nisiya ana ake, chifukwa mulibe udzu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Inde, mbawalanso ya m'thengo ibala nisiya ana ake, chifukwa mulibe udzu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mbaŵala yomwe ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa choti kulibe msipu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ngakhale mbawala yayikazi ikusiya mwana wake wakhanda ku thengo chifukwa kulibe msipu. Onani mutuwo |