Yeremiya 14:3 - Buku Lopatulika3 Akulu ao atuma ang'ono ao kumadzi; afika kumaenje, osapeza madzi; abwera ndi mitsuko yao yopanda kanthu; ali ndi manyazi, athedwa nzeru, afunda mitu yao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20143 Akulu ao atuma ang'ono ao kumadzi; afika kumaenje, osapeza madzi; abwera ndi mitsuko yao yopanda kanthu; ali ndi manyazi, athedwa nzeru, afunda mitu yao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa3 Atsogoleri ao otchuka akutuma antchito ao kuti akatunge madzi. Apita ku zitsime, koma osapezako madzi, ndiye akubwerera ndi mitsuko yopanda kanthu. Achita manyazi ndipo atha nzeru, adziphimba kumaso. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero3 Anthu awo wolemekezeka akutuma antchito awo kuti akatunge madzi. Apita ku zitsime osapezako madzi. Choncho amabwerera ndi mitsuko yopanda madzi. Amanyazi ndi othedwa nzeru adziphimba kumaso. Onani mutuwo |