Yeremiya 14:2 - Buku Lopatulika2 Yuda alira, ndipo zipata zake zilefuka, zikhala pansi zovekedwa ndi zakuda; mfuu wa Yerusalemu wakwera. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Yuda alira, ndipo zipata zake zilefuka, zikhala pansi zovekedwa ndi zakuda; mfuu wa Yerusalemu wakwera. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 “Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika, anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni. Kulira kwa anthu a mu Yerusalemu kwakula. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 “Yuda akulira, mizinda yake ikuvutika; anthu ake adzigwetsa pansi mwachisoni, kulira kwa Yerusalemu kwakula. Onani mutuwo |