Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti

- Zotsatsa -




Yeremiya 14:1 - Buku Lopatulika

1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya onena za chilala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

1 Mau a Yehova amene anadza kwa Yeremiya onena za chilala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

1 Ine Yeremiya Chauta adandiwuza mau onena za chilala, mau ake adati,

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

1 Awa ndi mawu amene Yehova anamuwuza Yeremiya onena za chilala:

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 14:1
4 Mawu Ofanana  

ndipo ndidzaupasula; sudzadzomboleredwa kapena kulimidwa; koma padzamera lunguzi ndi minga; ndidzalamuliranso mitambo kuti isavumbwepo mvula.


Ndipo adzakhala ngati mtengo wooka kuli madzi, wotambalitsa mizu yake pamtsinje, wosaopa pofika nyengo yadzuwa, koma tsamba lake likhala laliwisi; ndipo suvutika chaka cha chilala, suleka kubala zipatso.


Ndipo mvula yakanidwa, ndipo panalibe mvula ya masika; ndipo unali ndi nkhope ya mkazi wadama, unakana manyazi.


Mphulupulu zanu zachotsa zimenezi, ndi zochimwa zanu zakukanitsani inu zinthu zabwino.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa