Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 13:4 - Buku Lopatulika

4 Tenga mpango umene unaugula, umene uli m'chuuno mwako, nuuke, nupite ku Yufurate, nuubise m'menemo m'phanga la m'mwala.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Tenga mpango umene unaugula, umene uli m'chuuno mwako, nuuke, nupite ku Yufurate, nuubise m'menemo m'phanga la m'mwala.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 “Tenga mpango uja udagula nkuvala m'chiwuno mwakowu. Unyamuke nkupita msanga ku mtsinje wa Yufurate. Kumeneko ukabise mpangowo m'ming'alu yam'mathanthwe.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 “Tenga lamba amene unagula ndi kuvala mʼchiwuno mwako uja. Tsono pita ku mtsinje wa Yufurate ndipo ukamubise lambayo mʼmingʼalu ya mʼmatanthwe.”

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 13:4
5 Mawu Ofanana  

Ku mitsinje ya ku Babiloni, kumeneko tinakhala pansi, inde tinalira, pokumbukira Ziyoni.


Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine nthawi yachiwiri, kuti,


Imva zowawa, nuyesetse kubala, mwana wamkazi wa Ziyoni, ngati mkazi wakubala; pakuti udzatuluka m'mzinda tsopano, nudzakhala kuthengo, nudzafika ku Babiloni; komweko udzapulumutsidwa; komweko Yehova adzakuombola m'manja a adani ako.


Ndipo Yohane yekhayo anali nacho chovala chake cha ubweya wangamira, ndi lamba lachikopa m'chuuno mwake; ndi chakudya chake chinali dzombe ndi uchi wakuthengo.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa