Yeremiya 13:5 - Buku Lopatulika5 Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Tsono ndidapitadi kukaubisa mpangowo ku Yufurate, monga momwe Chauta adaandiwuzira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Ndipo ndinapitadi ndi kukabisa lambayo ku Yufurate, monga anenera Yehova. Onani mutuwo |