Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yeremiya 13:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo ndinapita, ndinaubisa pa Yufurate, monga Yehova anandiuza ine.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tsono ndidapitadi kukaubisa mpangowo ku Yufurate, monga momwe Chauta adaandiwuzira.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Ndipo ndinapitadi ndi kukabisa lambayo ku Yufurate, monga anenera Yehova.

Onani mutuwo Koperani




Yeremiya 13:5
10 Mawu Ofanana  

Anatero Mose; monga mwa zonse Yehova adamuuza, momwemo anachita.


Ndipo panali atapita masiku ambiri, kuti Yehova anati kwa ine, Uka, pita ku Yufurate, nukatenge kumeneko mpango uja, ndinakuuza iwe ukaubise kumeneko.


M'mwemo ndinanenera monga anandiuza, ndipo ponenera ine panali phokoso; ndipo taonani, panali gobedegobede, ndi mafupa anasendererana, fupa kutsata fupa linzake.


Umve zowawa pamodzi nane monga msilikali wabwino wa Khristu Yesu.


Ndi chikhulupiriro Abrahamu, poitanidwa, anamvera kutuluka kunka kumalo amene adzalandira ngati cholowa; ndipo anatuluka wosadziwa kumene akamukako.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa