Yeremiya 12:1 - Buku Lopatulika1 Wolungama ndinu, Yehova, pamene nditsutsana nanu mlandu; pokhapo ndinenane nanu za maweruzo; chifukwa chanji ipindula njira ya oipa? Chifukwa chanji akhala bwino onyengetsa? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20141 Wolungama ndinu, Yehova, pamene nditsutsana nanu mlandu; pokhapo ndinenane nanu za maweruzo; chifukwa chanji ipindula njira ya oipa? Chifukwa chanji akhala bwino onyengetsa? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa1 Inu Chauta nditati nditsutsane nanu, wokhoza ndinu ndithu. Komabe ndifuna kudandaulako kwa Inu za mlandu wanga. Chifukwa chiyani anthu oipa zinthu zimaŵayendera bwino? Chifukwa chiyani anthu osakhulupirika amakhala pabwino? Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero1 Yehova, Inu mumakhala wokhoza nthawi zonse ndikati nditsutsane nanu. Komabe ndikufuna kuyankhula nanu za mlandu wanga. Chifukwa chiyani anthu oyipa zinthu zimawayendera bwino? Chifukwa chiyani anthu achinyengo amakhala pabwino? Onani mutuwo |