Yeremiya 11:23 - Buku Lopatulika23 ndipo sadzakhala nao otsalira; pakuti ndidzatengera choipa pa anthu a ku Anatoti, chaka cha kulangidwa kwao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201423 ndipo sadzakhala nao otsalira; pakuti ndidzatengera choipa pa anthu a ku Anatoti, chaka cha kulangidwa kwao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa23 Sadzapulumuka ndi mmodzi yemwe, chifukwa ndidzaononga anthu a ku Anatoti, chikadzafika chaka chao cha chilango.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero23 Sipadzakhala otsala ndi mmodzi yemwe, chifukwa ndidzalanga anthu a ku Anatoti chikadzafika chaka chawo cha chilango.’ ” Onani mutuwo |