Yeremiya 12:2 - Buku Lopatulika2 Inu Mwabzala iwo, inde, anagwiritsatu mizu; amera, inde, abalatu zipatso; muli pafupi m'kamwa mwao, muli patali ndi impso zao. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Inu Mwabzala iwo, inde, anagwiritsatu mizu; amera, inde, abalatu zipatso; muli pafupi m'kamwa mwao, muli patali ndi impso zao. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Inu mudaŵabzala, ndipo adamera mizu. Amakula, namabala zipatso. Amakonda kulankhula za Inu, koma mitima yao ili kutali ndi Inu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Inu munawadzala ndipo anamera mizu; amakula ndi kubereka zipatso. Dzina lanu limakhala pakamwa pawo nthawi zonse, koma mitima yawo imakhala kutali ndi Inu. Onani mutuwo |