Yeremiya 1:11 - Buku Lopatulika11 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti, Yeremiya, uona chiyani? Ndipo ndinati, Ine ndiona nthyole ya katungurume. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201411 Ndipo mau a Yehova anadza kwa ine, kuti, Yeremiya, uona chiyani? Ndipo ndinati, Ine ndiona nthyole ya katungurume. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa11 Chauta adandifunsa kuti, “Yeremiya, kodi ukuwona chiyani?” Ine ndidayankha kuti, “Ndikuwona nthambi ya mtowo.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero11 Yehova anandifunsa kuti, “Yeremiya, kodi ukuona chiyani?” Ine ndinayankha kuti, “Ndikuona nthambi ya mtengo wa mtowo.” Onani mutuwo |