Yeremiya 1:10 - Buku Lopatulika10 penyatu, lero ndakuika ulamulire mitundu ya anthu ndi maufumu, kuti uzule, upasule, uononge, ugwetse, umange, ubzale. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 penyatu, lero ndakuika ulamulire mitundu ya anthu ndi maufumu, kuti uzule, upasule, uononge, ugwetse, umange, ubzale. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Ndikukuika lero kuti ukhale ndi ulamuliro pa maiko a anthu ndi maufumu ao, kuti uzule ndi kugwetsa, kuti uwononge ndi kugumula, kuti umange ndi kubzala.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Lero ndakusankha kuti ukhale ndi ulamuliro pa mitundu ya anthu ndi pa maufumu awo kuti uzule ndi kugwetsa, uwononge ndi kugumula, kuti uwamange ndi kudzala.” Onani mutuwo |