Yakobo 5:5 - Buku Lopatulika5 Mwadyerera padziko, ndipo mwachita zokukondweretsani; mwadyetsa mitima yanu m'tsiku lakupha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20145 Mwadyerera padziko, ndipo mwachita zokukondweretsani; mwadyetsa mitima yanu m'tsiku lakupha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa5 Mwakhala mukuchita maphwando, ndipo mwalidyera dziko lino lapansi. Mwadzinenepetsa pa tsiku lopha anthu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero5 Mwakhala pa dziko lapansi pano moyo ofewa ndipo mwalidyera dziko lapansi. Mwadzinenepetsa pa tsiku lokaphedwa. Onani mutuwo |