Yakobo 5:6 - Buku Lopatulika6 Munamtsutsa, munapha wolungamayo, iye sakaniza inu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Munamtsutsa, munapha wolungamayo, iye sakaniza inu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Mwamuweruza kuti ngwolakwa ndipo mwamupha munthu wolungama, iye osalimbalimba. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Mwaweruza kuti ndi wolakwa ndipo mwapha munthu wosalakwa, amene sakutsutsana nanu. Onani mutuwo |