Yakobo 1:9 - Buku Lopatulika9 Koma mbale woluluka adzitamandire pa ukulu wake; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20149 Koma mbale woluluka adzitamandire pa ukulu wake; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa9 Mbale woluluka anyadire pamene Mulungu amkweza. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero9 Abale omwe ndi anthu wamba anyadire pamene akwezedwa. Onani mutuwo |