Yakobo 1:8 - Buku Lopatulika8 munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha panjira zake zonse. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20148 munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha pa njira zake zonse. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa8 pakuti iyeyo ndi wa mitima iŵiri, ndi wosakhazikika pa zochita zake zonse. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero8 Iyeyu ndi munthu wa mitima iwiri, wosakhazikika pa zimene akuchita. Onani mutuwo |