Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yakobo 1:8 - Buku Lopatulika

8 munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha panjira zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

8 munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha pa njira zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

8 pakuti iyeyo ndi wa mitima iŵiri, ndi wosakhazikika pa zochita zake zonse.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

8 Iyeyu ndi munthu wa mitima iwiri, wosakhazikika pa zimene akuchita.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 1:8
13 Mawu Ofanana  

Ndipo Eliya anayandikira kwa anthu onse, nati, Mukayikakayika kufikira liti? Ngati Yehova ndiye Mulungu, mtsateni Iye; ngati Baala, mumtsate iyeyo. Ndipo panalibe ndi mmodzi yemwe anamuyankha.


Amaopa Yehova, namatumikiranso milungu yao, monga mwa miyambo ya amitundu anawachotsako.


Ndipo amitundu awa anaopa Yehova, natumikira mafano ao osema; ana ao omwe, ndi zidzukulu zao zomwe, monga anachita makolo ao, momwemo iwo omwe mpaka lero lino.


Ndidana nao a mitima iwiri; koma ndikonda chilamulo chanu.


Ndipo Ambuye anati, Popeza anthu awa ayandikira ndi Ine ndi m'kamwa mwao, nandilemekeza ndi milomo yao, koma mtima wao uli kutali ndi Ine, ndi mantha ao akundiopa Ine, ndi lamulo la anthu analiphunzira;


Mtima wao wagawikana, tsopano adzapezeka opalamula, adzapasula maguwa ao a nsembe, nadzaononga zoimiritsa zao.


Diso ndilo nyali ya thupi; chifukwa chake ngati diso lako lili la kumodzi, thupi lako lonse lidzakhala lowalitsidwa.


Palibe munthu angathe kukhala kapolo wa ambuye awiri: pakuti pena adzamuda mmodziyo, ndi kukonda winayo; pena adzakangamira kwa mmodzi, nadzanyoza wina. Simungathe kukhala kapolo wa Mulungu ndi wa Chuma.


Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye;


Yandikirani kwa Mulungu, ndipo adzayandikira kwa inu. Sambani m'manja, ochimwa inu; yeretsani mitima, a mitima iwiri inu.


okhala nao maso odzala ndi chigololo, osakhoza kuleka uchimo, kunyengerera iwo a moyo wosakhazikika; okhala nao mtima wozolowera kusirira; ana a temberero;


monganso m'makalata ake onse pokamba momwemo za izi; m'menemo muli zina zovuta kuzizindikira, zimene anthu osaphunzira ndi osakhazikika apotoza, monganso atero nao malembo ena, ndi kudziononga nao eni.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa