Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yakobo 1:7 - Buku Lopatulika

7 Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

7 Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

7 Munthu wotere asamaganiza kuti nkudzalandira kanthu kwa Ambuye ai;

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

7 Munthu wotere asayembekezere kulandira kalikonse kuchokera kwa Ambuye.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 1:7
7 Mawu Ofanana  

Nsembe ya oipa inyansa Yehova; koma pemphero la oongoka mtima limkondweretsa.


Nsembe ya oipa inyansa; makamaka pakudza nayo iwo mwachiwembu.


Ndipo pamene mutambasula manja anu, ndidzakubisirani inu maso anga; inde pochulukitsa mapemphero anu Ine sindidzamva; manja anu adzala mwazi.


Koma apemphe ndi chikhulupiriro, wosakayika konse; pakuti wokayikayo afanana ndi funde la nyanja lotengeka ndi mphepo ndi kuwinduka nayo.


munthu wa mitima iwiri akhala wosinkhasinkha panjira zake zonse.


Mupempha, ndipo simulandira, popeza mupempha koipa, kuti mukachimwaze pochita zikhumbitso zanu.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa