Yakobo 1:7 - Buku Lopatulika7 Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20147 Pakuti asayese munthu uyu kuti adzalandira kanthu kwa Ambuye; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa7 Munthu wotere asamaganiza kuti nkudzalandira kanthu kwa Ambuye ai; Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero7 Munthu wotere asayembekezere kulandira kalikonse kuchokera kwa Ambuye. Onani mutuwo |