Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Yakobo 1:23 - Buku Lopatulika

23 Pakuti ngati munthu ali wakumva mau, wosati wakuchita, iyeyu afanana ndi munthu wakuyang'anira nkhope yake ya chibadwidwe chake m'kalirole;

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

23 Pakuti ngati munthu ali wakumva mau, wosati wakuchita, iyeyu afanana ndi munthu wakuyang'anira nkhope yake ya chibadwidwe chake m'kalirole;

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

23 Paja munthu amene amangomva chabe mau, osachita zimene wamvazo, ali ngati munthu woyang'anira nkhope yake yachibadwa m'galasi.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

23 Munthu aliyense amene amangomva mawu koma osachita zimene mawuwo amanena, ali ngati munthu amene amayangʼana nkhope yake pa galasi.

Onani mutuwo Koperani




Yakobo 1:23
8 Mawu Ofanana  

Koma mau amene wanena ndi ife m'dzina la Yehova, sitidzakumvera iwe.


Munthu aliyense wakudza kwa Ine, ndi kumva mau anga, ndi kuwachita, ndidzakusonyezani amene afanana naye.


Ndipo alembi ndi Afarisi analikumzonda Iye, ngati adzachiritsa tsiku la Sabata; kuti akapeze chomneneza Iye.


Pakuti tsopano tipenya m'kalirole, ngati chimbuuzi; koma pomwepo maso ndi maso. Tsopano ndizindikira mderamdera; koma pomwepo ndidzazindikiratu, monganso ndazindikiridwa.


pakuti wadziyang'anira yekha, nachoka, naiwala pompaja nali wotani.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa