Yakobo 1:22 - Buku Lopatulika22 Khalani akuchita mau, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201422 Khalani akuchita mau, osati akumva okha, ndi kudzinyenga nokha. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa22 Musamadzinyenga pakungomva chabe mau a Mulungu, koma muzichita zimene mauwo anena. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero22 Musamangomvetsera chabe mawu, ndi kumadzinyenga nokha. Chitani zimene mawuwo amanena. Onani mutuwo |