Yakobo 1:24 - Buku Lopatulika24 pakuti wadziyang'anira yekha, nachoka, naiwala pompaja nali wotani. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201424 pakuti wadziyang'anira yekha, nachoka, naiwala pompaja nali wotani. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa24 Tsono amati akadzipenya, amachokapo, posachedwa nkuiŵalako m'mene akuwonekera. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero24 Akadziyangʼana amachoka, nthawi yomweyo nʼkuyiwala mmene akuonekera. Onani mutuwo |