Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 4:16 - Buku Lopatulika

16 Ndipo Naomi anamtenga mwanayo, namuika pachifuwa pake, nakhala mlezi wake.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndipo Naomi anamtenga mwanayo, namuika pachifuwa pake, nakhala mlezi wake.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Naomi adanyamula mwanayo namfukata ndipo adakhala mlezi wake.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Kenaka Naomi anatenga mwanayo namufukata ndipo anakhala mlezi.

Onani mutuwo Koperani




Rute 4:16
2 Mawu Ofanana  

Nakhale uyu wakukubwezera moyo, ndi wodyetsa ukalamba wako; pakuti mpongozi wako amene akukonda, amene aposa ana aamuna asanu ndi awiri kukuthandiza, anambala.


Ndi akazi anansi ake anamutcha dzina, ndi kuti, Kwa Naomi kwambadwira mwana; namutcha dzina lake Obedi; ndiye atate wa Yese atate wa Davide.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa