Rute 4:12 - Buku Lopatulika12 ndi nyumba yako inge nyumba ya Perezi, amene Tamara anambalira Yuda, ndi mbeu imene Yehova adzakupatsa ya namwali uyu. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 ndi nyumba yako inge nyumba ya Perezi, amene Tamara anambalira Yuda, ndi mbeu imene Yehova adzakupatsa ya namwali uyu. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Ana ako amene Chauta adzakupatse mwa mai ameneyu, adzamange banja longa la Perezi, amene Tamara adabalira Yuda.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ana amene Yehova adzakupatsa mwa mkaziyu adzamange banja lako kukhala la Perezi, amene Tamara anamubalira Yuda.” Onani mutuwo |