Rute 4:13 - Buku Lopatulika13 Momwemo Bowazi anatenga Rute, nakhala iye mkazi wake; ndipo analowa kwa iye; nalola Yehova kuti aime, ndipo anabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201413 Momwemo Bowazi anatenga Rute, nakhala iye mkazi wake; ndipo analowa kwa iye; nalola Yehova kuti aime, ndipo anabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa13 Choncho Bowazi adakwatira Rute, ndipo Chauta adadalitsa Ruteyo, mwakuti adatenga pathupi nabala mwana wamwamuna. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero13 Choncho Bowazi anakwatira Rute. Yehova anamudalitsa nakhala ndi pakati, ndipo anabereka mwana wamwamuna. Onani mutuwo |