Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 3:5 - Buku Lopatulika

5 Ndipo ananena naye, Zonse muzinena ndidzachita.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Ndipo ananena naye, Zonse muzinena ndidzachita.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Rute adayankha kuti, “Zonse mwanenazi ndichita.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Rute anayankha kuti, “Ndichita zonse zimene mwanena.”

Onani mutuwo Koperani




Rute 3:5
4 Mawu Ofanana  

Ananu, mverani akukubalani mwa Ambuye, pakuti ichi nchabwino.


Ana inu, mverani akubala inu m'zonse, pakuti ichi Ambuye akondwera nacho.


Ndipo kudzali, akagona, upenye apo ati agone, numuke, nuvundukule ku mapazi ake, nugone, ndi iyeyo adzakufotokozera zoyenera kuchita iwe.


Pamenepo anatsikira popunthirapo, nachita zonse monga umo mpongozi wake adamuuza.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa