Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 3:4 - Buku Lopatulika

4 Ndipo kudzali, akagona, upenye apo ati agone, numuke, nuvundukule ku mapazi ake, nugone, ndi iyeyo adzakufotokozera zoyenera kuchita iwe.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

4 Ndipo kudzali, akagona, upenye apo ati agone, numuke, nuvundukule ku mapazi ake, nugone, ndi iyeyo adzakufotokozera zoyenera kuchita iwe.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

4 Pamene akukagona, ukaonetsetse malo amene akagonewo. Tsono ukavundukule chofunda chake nukagona ku mapazi ake. Motero iyeyo akakuuza zoti uchite.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

4 Akamakagona, iwe ukaonetsetse malo amene wagonawo. Kenaka upite ndi kuvundukula chofunda ku mapazi ake ndi kugona. Iyeyo akakuwuza zoti uchite.”

Onani mutuwo Koperani




Rute 3:4
3 Mawu Ofanana  

Mupewe maonekedwe onse a choipa.


Usambe tsono, nudzole, nuvale zovala zako, nutsikire popunthirapo, koma usadziwike naye munthuyo, koma atatha kudya ndi kumwa ndiko.


Ndipo ananena naye, Zonse muzinena ndidzachita.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa