Rute 3:2 - Buku Lopatulika2 Nanga Bowazi wodziwana nafe, amene unakhala nao adzakazi ake? Taona, usiku uno apuntha barele popunthirapo. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20142 Nanga Bowazi wodziwana nafe, amene unakhala nao adzakazi ake? Taona, usiku uno apuntha barele popunthirapo. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa2 Bowazi amene adzakazi ake unali nawo, ndi wachibale wathu. Usiku uno iye akhala akupuntha barele ku malo ake opunthira. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero2 Bowazi amene adzakazi ake wakhala nawo nthawi yonseyi, si wachibale wathu kodi? Usiku uno akhala akupeta barele ku malo opunthira. Onani mutuwo |