Rute 3:12 - Buku Lopatulika12 Tsopano ndipo, zoonadi, ine ndine wakukuombolera cholowa, koma pali wakukuombolera woposa ine. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201412 Tsopano ndipo, zoonadi, ine ndine wakukuombolera cholowa, koma pali wakukuombolera woposa ine. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa12 Nzoona, ine ndine wachibale, komabe alipo wachibale weniweni kupambana ine. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero12 Ngakhale kuti ndinedi wachibale woyenera kukusamala, koma alipo wachibale weniweni kuposa ine. Onani mutuwo |