Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 3:11 - Buku Lopatulika

11 Ndipo tsopano, mwana wanga, usaope; ndidzakuchitira zonse unenazi; pakuti onse a pa mudzi wa anthu a mtundu wanga adziwa kuti iwe ndiwe mkazi waulemu.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

11 Ndipo tsopano, mwana wanga, usaope; ndidzakuchitira zonse unenazi; pakuti onse a pa mudzi wa anthu a mtundu wanga adziwa kuti iwe ndiwe mkazi waulemu.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

11 Tsopano usadandaule, mwana wanga. Ndidzakuchitira zonse zimene upemphe, pakuti anzanga am'mudzimu akudziŵa kuti ndiwe mkazi wabwino.

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

11 Ndipo tsopano mwana wanga usaope. Ine ndidzakuchitira chilichonse udzapemphe popeza anzanga onse amʼmudzi muno akudziwa kuti ndiwe mkazi wa khalidwe labwino.

Onani mutuwo Koperani




Rute 3:11
5 Mawu Ofanana  

Ndipo Yehova anamuonekera iye usiku womwewo, nati, Ine ndine Mulungu wa Abrahamu atate wako; usaope, chifukwa kuti Ine ndili ndi iwe, ndipo ndidzakudalitsa iwe, ndi kuchulukitsa mbeu zako, chifukwa cha Abrahamu kapolo wanga.


Mkazi wodekha ndiye korona wa mwamuna wake; koma wochititsa manyazi akunga chovunditsa mafupa a mwamunayo.


Mkazi wangwiro ndani angampeze? Pakuti mtengo wake uposa ngale.


Tsopano ndipo, zoonadi, ine ndine wakukuombolera cholowa, koma pali wakukuombolera woposa ine.


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa