Rute 2:6 - Buku Lopatulika6 Ndipo mnyamata woyang'anira ochekawo anayankha nati, Ndiye mkazi Mmowabuyo anabwera ndi Naomi ku dziko la Mowabu; Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 20146 Ndipo mnyamata woyang'anira ochekawo anayankha nati, Ndiye mkazi Mmowabuyo anabwera ndi Naomi ku dziko la Mowabu; Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa6 Kapitao wakeyo adayankha kuti, “Maiyu ndi Mmowabu amene adabwera ndi Naomi kuchokera ku dziko la Mowabu. Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero6 Kapitawo uja anayankha kuti, “Mayiyu ndi Mmowabu amene anabwera ndi Naomi kuchokera ku dziko la Mowabu. Onani mutuwo |