Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 2:5 - Buku Lopatulika

5 Nati Bowazi kwa mnyamata woyang'anira ochekawo, Mkazi uyu ngwa yani?

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

5 Nati Bowazi kwa mnyamata woyang'anira ochekawo, Mkazi uyu ngwa yani?

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

5 Tsono Bowazi adafunsa kapitao wake amene ankayang'anira anthu okolola aja kuti, “Kodi mai uyu ndani?”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

5 Bowazi anafunsa kapitawo wake amene ankayangʼanira okolola aja kuti, “Mayi uyo ndi ndani?”

Onani mutuwo Koperani




Rute 2:5
4 Mawu Ofanana  

Ndipo taona, Bowazi anafuma ku Betelehemu, nati kwa ocheka, Yehova akhale nanu. Namyankha iwo, Yehova akudalitseni.


Ndipo mnyamata woyang'anira ochekawo anayankha nati, Ndiye mkazi Mmowabuyo anabwera ndi Naomi ku dziko la Mowabu;


ndi Salimoni anabala Bowazi, ndi Bowazi anabala Obedi;


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa