Biblia Todo Logo
Baibulo la pa intaneti
- Zotsatsa -




Rute 2:16 - Buku Lopatulika

16 Ndiponso mumtayire za m'manja, ndi kuzisiya, natole khunkha, osamdzudzula.

Onani mutuwo Koperani

Chichewa Buku Lopatulika Bible 2014

16 Ndiponso mumtayire za m'manja, ndi kuzisiya, natole khunkha, osamdzudzula.

Onani mutuwo Koperani

Buku Loyera Catholic Edition - Chichewa

16 Muzimusololerako ngala zina zam'mitolo ndi kumlekera kuti azikunkha, osamdzudzula.”

Onani mutuwo Koperani

Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero

16 Koma muzimusololerako ngala zina za mʼmitolo ndi kumusiyira kuti azikunkha ndipo musamukalipire.”

Onani mutuwo Koperani




Rute 2:16
11 Mawu Ofanana  

Anagawagawa, anapatsa aumphawi; chilungamo chake chikhalitsa kosatha; nyanga yake idzakwezeka ndi ulemu.


Wochitira waumphawi chifundo abwereka Yehova; adzambwezera chokoma chakecho.


Ndipo Mfumuyo idzayankha nidzati kwa iwo, Indetu ndinena kwa inu, Chifukwa munachitira ichi mmodzi wa abale anga, ngakhale ang'onong'ono awa, munandichitira ichi Ine.


Patsani zosowa oyera mtima; cherezani aulendo.


Pakuti ndinali nacho chimwemwe chambiri ndi chisangalatso pa chikondi chako, popeza mitima ya oyera mtima yatsitsimuka mwa iwe, mbale.


pakuti Mulungu sali wosalungama kuti adzaiwala ntchito yanu, ndi chikondicho mudachionetsera kudzina lake, umo mudatumikira oyera mtima ndi kuwatumikirabe.


Ndipo ataumirira kukatola khunkha, Bowazi analamulira anyamata ake ndi kuti, Atole khunkha ngakhale pakati pa mitolo, musamchititse manyazi.


Natola khunkha iye m'munda mpaka madzulo; naomba khunkhalo; napeza ngati efa wa barele,


Titsatireni:

Zotsatsa


Zotsatsa