Rute 2:16 - Buku Lopatulika16 Ndiponso mumtayire za m'manja, ndi kuzisiya, natole khunkha, osamdzudzula. Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201416 Ndiponso mumtayire za m'manja, ndi kuzisiya, natole khunkha, osamdzudzula. Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa16 Muzimusololerako ngala zina zam'mitolo ndi kumlekera kuti azikunkha, osamdzudzula.” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero16 Koma muzimusololerako ngala zina za mʼmitolo ndi kumusiyira kuti azikunkha ndipo musamukalipire.” Onani mutuwo |