Rute 2:10 - Buku Lopatulika10 Potero anagwa nkhope yake pansi, nadziweramira pansi, nanena naye, Mwandikomera mtima chifukwa ninji kuti mundisamalira ine, popeza ndine mlendo? Onani mutuwoChichewa Buku Lopatulika Bible 201410 Potero anagwa nkhope yake pansi, nadziweramira pansi, nanena naye, Mwandikomera mtima chifukwa ninji kuti mundisamalira ine, popeza ndine mlendo? Onani mutuwoBuku Loyera Catholic Edition - Chichewa10 Rute adaŵerama, nazyolikitsa nkhope pansi, ndipo adafunsa kuti, “Chifukwa chiyani ndapeza kukoma mtima kotereku mwa inu, kuti mulabadeko za ine mlendo?” Onani mutuwoMawu a Mulungu mu Chichewa Chalero10 Atamva zimenezi Rute anawerama nazolikitsa nkhope yake pansi. Kenaka anafunsa kuti, “Mwandikomera mtima chotere mlendo ngati ine chifukwa chiyani?” Onani mutuwo |